Lyrics | New Lyrics | Artists: M | National Anthem lyrics | Malawi Native Anthem Text lyrics
National Anthem Malawi Native Anthem Text lyrics
Malawi Native Anthem Text MP3 ringtone
National Anthem Malawi Native Anthem Text video
This content requires the Adobe Flash Player.
Get Flash
Malawi Native Anthem Text MP3 ringtone
1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco
Back to: National Anthem lyrics
These lyrics are not available for printing.
Malawi Native Anthem Text MP3 ringtone
New Lyrics DOT DOT DOT He Doesn't Have To Know lyricsDOT DOT DOT Smile lyricsDOT DOT DOT Gravity lyricsD-PRYDE Bottom Dollar lyricsDOT DOT DOT You Do lyricsREH DOGG Comparing Past Lovers lyricsDOT DOT DOT All Be Alright lyricsNEIL TACULOD Life Is Short lyricsCHRIS BROWN Off That Liquor lyricsSTORM CORROSION Hag lyrics